Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 8:2 - Buku Lopatulika

Ndipo ukakana kuwalola amuke, taona, Ine ndidzapanda dziko lako lonse ndi achule;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ukakana kuwalola amuke, taona, Ine ndidzapanda dziko lako lonse ndi achule;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ukakana kuŵalola, dziko lako lonse ndidzalilanga polidzaza ndi achule.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo ngati simulola kuti apite Ine ndidzalanga dziko lonse la Igupto polidzaza ndi achule.

Onani mutuwo



Eksodo 8:2
7 Mawu Ofanana  

Dziko lao linachuluka achule, m'zipinda zomwe za mafumu ao.


Anawatumizira pakati pao mitambo ya ntchentche zakuwatha; ndi achule akuwaononga.


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, Walemera mtima wa Farao, akana kulola anthu apite.


Ndipo Yehova anati kwa Mose, Lowa kwa Farao, nunene naye, Atero Yehova, Lola anthu anga amuke, kuti anditumikire.


ndipo m'mtsinjemo mudzachuluka achule, amene adzakwera nadzalowa m'nyumba mwako, ndi m'chipinda chogona iwe, ndi pakama pako, ndi m'nyumba ya anyamata ako, ndi pa anthu ako, m'michembo yanu yootcheramo, ndi m'mbale zanu zoumbiramo.


Pakuti ukakana kuwalola amuke, ndi kuwagwira chigwiritsire,