Eksodo 7:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, Walemera mtima wa Farao, akana kulola anthu apite. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, Walemera mtima wa Farao, akana kulola anthu apite. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Tsono Chauta adauza Mose kuti, “Farao ndi wokanika kwambiri, akukana kulola anthu anga kuti apite. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Kenaka Yehova anati kwa Mose, “Farao ndi wowuma mtima. Akukana kulola anthu anga kuti apite. Onani mutuwo |