Eksodo 7:13 - Buku Lopatulika13 Koma mtima wa Farao unalimba, ndipo sanamvere iwo; monga adalankhula Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Koma mtima wa Farao unalimba, ndipo sanamvere iwo; monga adalankhula Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Farao adaumabe mtima, ndipo sadasamale zimene ankamuuzazo monga momwe Chauta adaanenera muja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Koma mtima wa Farao unawuma ndipo sanawamvere monga momwe Yehova ananenera. Onani mutuwo |