Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 6:22 - Buku Lopatulika

Ndi ana aamuna a Uziyele ndiwo: Misaele, ndi Elizafani, ndi Sitiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi ana amuna a Uziyele ndiwo: Misaele, ndi Elizafani, ndi Sitiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ana a Uziyele naŵa: Misaele, Elizafani ndi Sitiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ana a Uzieli anali Misaeli, Elizafani ndi Sitiri.

Onani mutuwo



Eksodo 6:22
5 Mawu Ofanana  

a ana a Elizafani, Semaya mkulu wao, ndi abale ake mazana awiri;


ndi a ana a Elizafani, Simiri ndi Yeuwele; ndi a ana a Asafu, Zekariya ndi Mataniya;


Potsatizana naye Baruki mwana wa Zabai anafulumira kukonza gawo lina kuyambira popindirira mpaka kukhomo la nyumba ya Eliyasibu mkulu wa ansembe.


Ndipo Mose anaitana Misaele ndi Elizafani, ana a Uziyele, mbale wa atate wa Aroni, nanena nao, Senderani pafupi, nyamulani abale anu muwachotse pakhomo pa malo opatulika kunka nao kunja kwa chigono.


Ndipo kalonga wa nyumba ya makolo ao ya mabanja a Akohati ndiye Elizafani mwana wa Uziyele.