Numeri 3:30 - Buku Lopatulika30 Ndipo kalonga wa nyumba ya makolo ao ya mabanja a Akohati ndiye Elizafani mwana wa Uziyele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Ndipo kalonga wa nyumba ya makolo ao ya mabanja a Akohati ndiye Elizafani mwana wa Uziyele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 pamodzi ndi Elizafani, mwana wa Uziyele, amene anali mutu wa mabanja a Akohati, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Mtsogoleri wa magulu a mabanja a Kohati anali Elizafani mwana wa Uzieli. Onani mutuwo |