Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 6:21 - Buku Lopatulika

Ndi ana aamuna a Izihara ndiwo: Kora ndi Nefegi, ndi Zikiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi ana amuna a Izihara ndiwo: Kora ndi Nefegi, ndi Zikiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ana a Izihara naŵa: Kora, Nefegi ndi Zikiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ana a Izihari anali Kora, Nefegi ndi Zikiri.

Onani mutuwo



Eksodo 6:21
7 Mawu Ofanana  

Ana a Kohati: Aminadabu mwana wake, Kora mwana wake, Asiri mwana wake,


ndi wotsatana naye Amasiya mwana wa Zikiri, wodzipereka kwa Yehova mwaufulu, ndi pamodzi ndi iye ngwazi zamphamvu zikwi mazana awiri;


Ndipo ana aamuna a Kora ndiwo: Asiri ndi Elikana, ndi Abiyasafu; amenewo ndiwo mabanja a Akora.


Koma Kora, mwana wa Izihara, mwana wa Kohati, mwana wa Levi, anatenga Datani ndi Abiramu, ana a Eliyabu, ndi Oni mwana wa Peleti, ana a Rubeni;


ndi dziko linayasama pakamwa pake ndi kuwameza, iwo ndi mabanja ao, ndi amuna ao onse akutsata Kora, ndi akatundu ao onse.