Numeri 16:32 - Buku Lopatulika32 ndi dziko linayasama pakamwa pake ndi kuwameza, iwo ndi mabanja ao, ndi amuna ao onse akutsata Kora, ndi akatundu ao onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 ndi dziko linayasama pakamwa pake ndi kuwameza, iwo ndi mabanja ao, ndi amuna ao onse akutsata Kora, ndi akatundu ao onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Nthakayo idayasama ndi kuŵameza onsewo pamodzi ndi mabanja ao ndiponso anthu onse a gulu la Kora ndi zinthu zao zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 ndipo dziko linatsekula pakamwa pake ndi kuwameza pamodzi ndi nyumba zawo ndi anthu onse a Kora ndi katundu wawo yense. Onani mutuwo |