Numeri 16:31 - Buku Lopatulika31 Ndipo kunali, pakutha iye kunena mau awa onse, nthaka inang'ambika pansi pao; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Ndipo kunali, pakutha iye kunena mau awa onse, nthaka inang'ambika pansi pao; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Mose atangomaliza kulankhula mau ameneŵa, nthaka idang'ambika pamene padaali iwopo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Atangotsiriza kuyankhula zimenezi, nthaka ya pamene anayimapo inagawikana Onani mutuwo |