Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 16:31 - Buku Lopatulika

31 Ndipo kunali, pakutha iye kunena mau awa onse, nthaka inang'ambika pansi pao;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Ndipo kunali, pakutha iye kunena mau awa onse, nthaka inang'ambika pansi pao;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Mose atangomaliza kulankhula mau ameneŵa, nthaka idang'ambika pamene padaali iwopo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Atangotsiriza kuyankhula zimenezi, nthaka ya pamene anayimapo inagawikana

Onani mutuwo Koperani




Numeri 16:31
9 Mawu Ofanana  

Dziko lapansi lasweka ndithu, dziko lapansi lasungunukadi, dziko lapansi lili kugwedezeka kopambana.


Koma Yehova akalenga chinthu chatsopano, ndi nthaka ikayasama pakamwa pake, nikawameza ndi zonse ali nazo, nakatsikira iwo kumanda ali ndi moyo; pamenepo mudzadziwa kuti anthu awa anyoza Mulungu.


ndi dziko linayasama pakamwa pake ndi kuwameza, iwo ndi mabanja ao, ndi amuna ao onse akutsata Kora, ndi akatundu ao onse.


Ndipo anthu anatsutsana ndi Mose, nanena, nati, Mwenzi titangomwalira muja abale athu anamwalira pamaso pa Yehova!


Atate wathu adamwalira m'chipululu, ndipo sanakhale iye pakati pa msonkhano wa iwo akusonkhana kutsutsana ndi Yehova, mu msonkhano wa Kora; koma anafera zoipa zakezake; ndipo analibe ana aamuna.


ndi chimene anachitira Datani ndi Abiramu, ana a Eliyabu, mwana wa Rubeni; muja nthaka inatsegula pakamwa pake, ndi kuwameza iwo, ndi mabanja ao, ndi mahema ao, ndi za moyo zonse zakuwatsata pakati pa Israele wonse.


Tsoka kwa iwo! Pakuti anayenda m'njira ya Kaini, ndipo anadziononga m'chisokero cha Balamu chifukwa cha kulipira, natayika m'chitsutsano cha Kora.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa