Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 6:22 - Buku Lopatulika

22 Ndi ana aamuna a Uziyele ndiwo: Misaele, ndi Elizafani, ndi Sitiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Ndi ana amuna a Uziyele ndiwo: Misaele, ndi Elizafani, ndi Sitiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Ana a Uziyele naŵa: Misaele, Elizafani ndi Sitiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Ana a Uzieli anali Misaeli, Elizafani ndi Sitiri.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 6:22
5 Mawu Ofanana  

a ana a Elizafani, Semaya mkulu wao, ndi abale ake mazana awiri;


ndi a ana a Elizafani, Simiri ndi Yeuwele; ndi a ana a Asafu, Zekariya ndi Mataniya;


Potsatizana naye Baruki mwana wa Zabai anafulumira kukonza gawo lina kuyambira popindirira mpaka kukhomo la nyumba ya Eliyasibu mkulu wa ansembe.


Ndipo Mose anaitana Misaele ndi Elizafani, ana a Uziyele, mbale wa atate wa Aroni, nanena nao, Senderani pafupi, nyamulani abale anu muwachotse pakhomo pa malo opatulika kunka nao kunja kwa chigono.


Ndipo kalonga wa nyumba ya makolo ao ya mabanja a Akohati ndiye Elizafani mwana wa Uziyele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa