Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 4:29 - Buku Lopatulika

Pamenepo Mose ndi Aroni anamuka nasonkhanitsa akulu onse a ana a Israele;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo Mose ndi Aroni anamuka nasonkhanitsa akulu onse a ana a Israele;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero Mose ndi Aroni adapita, nakasonkhanitsa atsogoleri onse a Aisraele.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mose ndi Aaroni anapita kukasonkhanitsa pamodzi akuluakulu onse a Aisraeli.

Onani mutuwo



Eksodo 4:29
5 Mawu Ofanana  

Anatuma Mose mtumiki wake, ndi Aroni amene adamsankha.


Ndipo Mose anadza, naitana akulu a anthu, nawaikira pamaso pao mau awa onse amene Yehova adamuuza.


Ndipo Iye ananena ndi Mose, Ukwere kudza kwa Yehova, iwe ndi Aroni, Nadabu ndi Abihu, ndi akulu a Israele makumi asanu ndi awiri; ndipo mugwadire pakudza kutali;


Koma sanatulutse dzanja lake pa akulu a ena a Israele; ndipo anapenya Mulungu, nadya, namwa.


Muka, nukasonkhanitse akulu a Israele, nunene nao, Yehova, Mulungu wa makolo anu anandionekera ine, Mulungu wa Abrahamu, Isaki ndi Yakobo, ndi kuti, Ndakuzondani ndithu, ndi kuona chomwe akuchitirani mu Ejipito;