Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 38:6 - Buku Lopatulika

Napanga mphiko za mtengo wakasiya, nazikuta ndi mkuwa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Napanga mphiko za mtengo wakasiya, nazikuta ndi mkuwa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adasema mphiko zonyamulira za mtengo wa kasiya, nazikuta ndi mkuŵa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anapanga nsichi zamtengo wa mkesha ndipo anazikuta ndi mkuwa.

Onani mutuwo



Eksodo 38:6
5 Mawu Ofanana  

ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;


mafuta akuunikira, zonunkhira za mafuta odzoza, ndi za chofukiza cha fungo lokoma;


Ndipo anayengera mathungo anai a sefa wamkuwayo mphete zinai, zikhale zopisamo mphiko.


Ndipo anapisa mphikozo mu mphetezo pa mbali za guwa la nsembe, kulinyamulira nazo; analipanga ndi matabwa, lagweregwere.


Potero ndinapanga likasa la mtengo wakasiya, ndinasemanso magome awiri amiyala onga oyamba aja, ndi kukwera m'phirimo, magome awiri ali m'manja mwanga.