Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 37:4 - Buku Lopatulika

Ndipo anapanga mphiko za mtengo wakasiya, nazikuta ndi golide.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anapanga mphiko za mtengo wakasiya, nazikuta ndi golide.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adapanga mphiko zinai za matabwa a mtengo wa kasiya, nazikuta ndi golide,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka anapanga mizati yamtengo wa mkesha ndi kuzikuta ndi golide.

Onani mutuwo



Eksodo 37:4
8 Mawu Ofanana  

Ndipo mphikozo zinatalika kuti nsonga za mphiko zidaoneka ku malo opatulika chakuno cha chipinda chamkati; koma sizinaoneke kubwalo; ndipo zikhala pomwepo mpaka lero lino.


ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;


Ndipo analiyengera mphete zinai zagolide pa miyendo yake inai; mphete ziwiri pa mbali yake imodzi, ndi mphete ziwiri pa mbali yake ina.


Ndipo anapisa mphiko m'mphetezo pa mbali zake za likasalo, kuti anyamulire nazo likasa.


Koma Ambuye anati kwa iye, Pita; pakuti iye ndiye chotengera changa chosankhika, chakunyamula dzina langa pamaso pa amitundu ndi mafumu ndi ana a Israele;


kuti mayesedwe a chikhulupiriro chanu, ndiwo a mtengo wake woposa wa golide amene angotayika, ngakhale ayesedwa ndi moto, akapezedwe ochitira chiyamiko ndi ulemerero ndi ulemu pa vumbulutso la Yesu Khristu;