Eksodo 37:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo anapisa mphiko m'mphetezo pa mbali zake za likasalo, kuti anyamulire nazo likasa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo anapisa mphiko m'mphetezo pa mbali zake za likasalo, kuti anyamulire nazo likasa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 ndipo mphikozo adazipisa m'mphete zija pa mbali zonse ziŵiri za bokosilo, kuti azinyamulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndipo analowetsa nsichizo mʼmphete zija za mbali zonse ziwiri za bokosilo kuti azinyamulira. Onani mutuwo |