Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 31:8 - Buku Lopatulika

ndi gomelo ndi zipangizo zake, ndi choikaponyali choona ndi zipangizo zake, ndi guwa la nsembe lofukizapo;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi gomelo ndi zipangizo zake, ndi choikapo nyali choona ndi zipangizo zake, ndi guwa la nsembe lofukizapo;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

tebulo ndi zipangizo zake, choikaponyale cha golide wabwino kwambiri, pamodzi ndi zipangizo zake, guwa lofukizirapo lubani,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

tebulo ndi zida zake, choyikapo nyale cha golide wabwino kwambiri ndi ziwiya zake zonse, guwa lofukizirapo lubani,

Onani mutuwo



Eksodo 31:8
5 Mawu Ofanana  

Akonze nyalizo pa choikaponyali choona pamaso pa Yehova nthawi zonse.


Kapena sayatsa nyali, ndi kuivundikira m'mbiya, koma aiika iyo pa choikapo chake; ndipo iunikira onse ali m'nyumbamo.