Levitiko 24:4 - Buku Lopatulika4 Akonze nyalizo pa choikaponyali choona pamaso pa Yehova nthawi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Akonze nyalizo pa choikapo nyali choona pamaso pa Yehova nthawi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Aroni ayatse nyale zimene zili pa choikapo chake cha golide wabwino kwambiri, kuti zikhale zoyaka nthaŵi zonse pamaso pa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Aaroni ayatse nyale zimene zili pa choyikapo nyale chagolide wabwino kwambiri kuti zikhale zoyaka nthawi zonse pamaso pa Yehova. Onani mutuwo |