Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 26:21 - Buku Lopatulika

makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi, ndi makamwa awiri pansi pa thabwa lina.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi, ndi makamwa awiri pansi pa thabwa lina.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndi masinde makumi anai asiliva, aŵiri pa fulemu lililonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Upangenso matsinde 40 asiliva, awiri pansi pa feremu iliyonse.

Onani mutuwo



Eksodo 26:21
3 Mawu Ofanana  

ndi pa mbali yake ina ya chihema, mbali ya kumpoto, pakhale matabwa makumi awiri; ndi makamwa asiliva makumi anai;


Ndipo uzipanga matabwa asanu ndi limodzi kwa mbali ya chihema cha kumbuyo.


Ndipo matalente zana limodzi a siliva ndiwo a kuyengera makamwa a malo opatulika, ndi makamwa a nsalu yotchinga; makamwa zana limodzi matalente zana limodzi, talente limodzi kamwa limodzi.