Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 26:15 - Buku Lopatulika

Ndipo uzipangira chihema matabwa oimirika, a mtengo wakasiya.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo uzipangira Kachisi matabwa oimirika, a mtengo wakasiya.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Upange mafulemu a chihemacho ndi matabwa oimirira bwino a mtengo wa kasiya.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Upange maferemu amatabwa amtengo wa mkesha oyimikira chihemacho.

Onani mutuwo



Eksodo 26:15
8 Mawu Ofanana  

ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;


Utali wake wa thabwa limodzi ndiwo mikono khumi, ndi kupingasa kwake kwa thabwali mkono ndi hafu.


Ndipo uzipanga matabwa a chihema, matabwa makumi awiri ku mbali ya kumwera, kumwera.