Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 26:16 - Buku Lopatulika

16 Utali wake wa thabwa limodzi ndiwo mikono khumi, ndi kupingasa kwake kwa thabwali mkono ndi hafu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Utali wake wa thabwa limodzi ndiwo mikono khumi, ndi kupingasa kwake kwa thabwali mkono ndi hafu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Muutali mwake fulemu lililonse likhale mamita anai ndi theka, ndipo muufupi mwake masentimita 69.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Feremu iliyonse ikhale yotalika mamita anayi ndipo mulifupi mwake mukhale masentimita 69.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 26:16
2 Mawu Ofanana  

Ndipo uzipangira chihema matabwa oimirika, a mtengo wakasiya.


Pa thabwa limodzi pakhale mitsukwa iwiri, yomangika pamodzi; uzitero pa matabwa onse a chihema.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa