Eksodo 26:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo uzipangira hema chophimba cha zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi chophimba za zikopa za akatumbu pamwamba pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo uzipangira hema chophimba cha zikopa za nkhosa zamphongo zonika zofiira, ndi chophimba za zikopa za akatumbu pamwamba pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Lona lija ulipangire chophimbira chake chofiira cha chikopa cha nkhosa zamphongo. Pambuyo pake upangenso chophimbira chotsiriza cha zikopa zofeŵa chodzayala pamwamba pa zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Upange chikopa cha nkhosa zazimuna cha utoto wofiira chophimbira tentiyo ndipo pamwamba pake upangireponso chophimbira china cha zikopa za akatumbu. Onani mutuwo |