Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 23:4 - Buku Lopatulika

Ukakomana ndi ng'ombe kapena bulu wa mdani wako zilinkusokera, uzimbwezera izo ndithu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ukakomana ndi ng'ombe kapena bulu wa mdani wako zilimkusokera, uzimbwezera izo ndithu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Ukaona ng'ombe ya mdani wako ikusokera, kapena bulu wake, utenge ukampatse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Ngati ukumana ndi ngʼombe kapena bulu wa mdani wako zitasochera, uwonetsetse kuti wazitenga kupita nazo kwa mwini wakeyo.

Onani mutuwo



Eksodo 23:4
9 Mawu Ofanana  

Mdani wako akamva njala umdyetse, akamva ludzu ummwetse madzi.


kapena anapeza chinthu chotayika, nanenapo bodza, nalumbira pabodza; pa chimodzi cha izi zonse amachita munthu, ndi kuchimwapo;


koma Ine ndinena kwa inu, Kondanani nao adani anu, ndi kupempherera iwo akuzunza inu;


Penyani kuti wina asabwezere choipa womchitira choipa; komatu nthawi zonse mutsatire chokoma, kwa anzanu, ndi kwa onse.