Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 16:36 - Buku Lopatulika

Koma omeri ndilo limodzi la magawo khumi la efa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma omeri ndilo limodzi la magawo khumi la efa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Malita aŵiri alingana ndi gawo lachikhumi la efa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

(Malita awiri amafanana ndi gawo lakhumi la efa).

Onani mutuwo



Eksodo 16:36
5 Mawu Ofanana  

Amenewo ndiwo mau walamulira Yehova, Aoleko yense monga mwa njala yake; munthu mmodzi omeri limodzi, monga momwe muli, yense atengere iwo m'hema mwake.


Efa ndi bati zikhale za muyeso umodzi, bati liyese limodzi la magawo khumi la homeri, efa lomwe liyese limodzi la magawo khumi la homeri; muyeso wao uyesedwa monga mwa homeri.


ndi limodzi la magawo khumi la efa wa ufa wosalala ukhale nsembe yaufa, wosakaniza ndi limodzi la magawo anai la hini wa mafuta opera.


Natola khunkha iye m'munda mpaka madzulo; naomba khunkhalo; napeza ngati efa wa barele,