Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Rute 2:17 - Buku Lopatulika

17 Natola khunkha iye m'munda mpaka madzulo; naomba khunkhalo; napeza ngati efa wa barele,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Natola khunkha iye m'munda mpaka madzulo; naomba khunkhalo; napeza ngati efa wa barele,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Choncho Rute adakunkha m'mundamo mpaka madzulo. Pambuyo pake adapuntha barele amene adakunkha uja, ndipo adakwanira pafupi makilogramu khumi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Choncho Rute anakunkha mʼmundamo mpaka madzulo. Kenaka anapuntha barele anakunkhayo, ndipo anakwanira pafupifupi makilogalamu khumi.

Onani mutuwo Koperani




Rute 2:17
5 Mawu Ofanana  

Koma omeri ndilo limodzi la magawo khumi la efa.


Ayang'anira mayendedwe a banja lake, sadya zakudya za ulesi.


Ndiponso mumtayire za m'manja, ndi kuzisiya, natole khunkha, osamdzudzula.


nalisenza nalowa kumzinda; ndipo mpongozi wake anaona khunkhalo; Rute natulutsanso nampatsa mkute uja anausiya atakhuta.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa