Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 16:19 - Buku Lopatulika

Ndipo Mose ananena nao, Palibe munthu asiyeko kufikira m'mawa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Mose ananena nao, Palibe munthu asiyeko kufikira m'mawa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo Mose adaŵauza kuti, “Munthu aliyense asasungeko mpaka m'maŵa.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Mose anawawuza kuti, “Wina aliyense asasunge mpaka mmawa.”

Onani mutuwo



Eksodo 16:19
5 Mawu Ofanana  

Ndipo musasiyako kufikira m'mawa; koma yotsalira kufikira m'mamawayo muipsereze ndi moto.


Koma sanammvere Mose; ndipo ena anasiyako kufikira m'mawa; koma unagwa mphutsi, nununkha. Ndipo Mose anakwiya nao.


Ndipo ananena nao, Ichi ndi chomwe Yehova analankhula, Mawa ndiko kupuma, Sabata lopatulika la Yehova; chimene muziotcha, otchani, ndi chimene muziphika phikani; ndi chotsala chikukhalireni chosungika kufikira m'mawa.


Usapereka mwazi wa nsembe yanga pamodzi ndi mkate wa chotupitsa; ndi mafuta a madyerero anga asagonamo kufikira m'mawa.


Chifukwa chake musadere nkhawa za mawa; pakuti mawa adzadzidera nkhawa iwo okha. Zikwanire tsiku zovuta zake.