Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 16:16 - Buku Lopatulika

Amenewo ndiwo mau walamulira Yehova, Aoleko yense monga mwa njala yake; munthu mmodzi omeri limodzi, monga momwe muli, yense atengere iwo m'hema mwake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Amenewo ndiwo mau walamulira Yehova, Aoleko yense monga mwa njala yake; munthu mmodzi omeri limodzi, monga momwe muli, yense atengere iwo m'hema mwake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta walamula kuti aliyense mwa inu atole womukwanira kudya, ndiye kuti malita aŵiri pa munthu mmodzi, malinga ndi chiŵerengero cha anthu onse a m'hema mwake.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yehova walamula kuti, ‘Aliyense atole zomukwanira kudya, malita awiri pa munthu mmodzi molingana ndi chiwerengero cha anthu amene ali mu tenti yanu.’ ”

Onani mutuwo



Eksodo 16:16
4 Mawu Ofanana  

Ndipo ana a Israele anatero, naola wina wambiri, wina pang'ono.


Ndipo pamene anayesa ndi omeri, iye amene adaola wambiri sunamtsalire, ndi iye amene adaola pang'ono sunamsowe; yense anaola monga mwa njala yake.


Koma omeri ndilo limodzi la magawo khumi la efa.