Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 16:36 - Buku Lopatulika

36 Koma omeri ndilo limodzi la magawo khumi la efa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Koma omeri ndilo limodzi la magawo khumi la efa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Malita aŵiri alingana ndi gawo lachikhumi la efa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 (Malita awiri amafanana ndi gawo lakhumi la efa).

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 16:36
5 Mawu Ofanana  

Amenewo ndiwo mau walamulira Yehova, Aoleko yense monga mwa njala yake; munthu mmodzi omeri limodzi, monga momwe muli, yense atengere iwo m'hema mwake.


Efa ndi bati zikhale za muyeso umodzi, bati liyese limodzi la magawo khumi la homeri, efa lomwe liyese limodzi la magawo khumi la homeri; muyeso wao uyesedwa monga mwa homeri.


ndi limodzi la magawo khumi la efa wa ufa wosalala ukhale nsembe yaufa, wosakaniza ndi limodzi la magawo anai la hini wa mafuta opera.


Natola khunkha iye m'munda mpaka madzulo; naomba khunkhalo; napeza ngati efa wa barele,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa