Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 14:1 - Buku Lopatulika

Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Chauta adalamula Mose kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka Yehova anati kwa Mose,

Onani mutuwo



Eksodo 14:1
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni m'dziko la Ejipito, ndi kuti,


Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi kuti,


sanachotse mtambo usana, kapena mtambo wamoto usiku, pamaso pa anthu.


Lankhula ndi anthu a Israele, kuti abwerere m'mbuyo nagone patsogolo pa Pihahiroti, pakati pa Migidoli ndi nyanja, patsogolo pa Baala-Zefoni; pandunji pake mugone panyanja.


Ndipo anachokera ku Etamu, nayenda nabwerera ku Pihahiroti, ndiko kutsogolo kwake kwa Baala-Zefoni; namanga iwo patsogolo pa Migidoli.


Ndipo ndinatulutsa atate anu mu Ejipito; ndipo munadza kunyanja; koma Aejipito analondola atate anu ndi magaleta ndi apakavalo mpaka ku Nyanja Yofiira.