Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 14:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Kenaka Yehova anati kwa Mose,

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Tsono Chauta adalamula Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 14:1
6 Mawu Ofanana  

Yehova anayankhula kwa Mose ndi Aaroni mʼdziko la Igupto kuti,


Yehova anati kwa Mose,


Usana, chipilala cha mtambo ndi usiku, chipilala cha moto zinali patsogolo kuwatsogolera anthu aja.


“Uza Aisraeli abwerere ndi kukagona pafupi ndi Pihahiroti, pakati pa Migidoli ndi nyanja. Inu mumange zithando mʼmbali mwa nyanja moyangʼanana ndi Baala-Zefoni.


Ndipo atachoka ku Etamu, anabwerera ku Pihahiroti, kummawa kwa Baala-Zefoni, ndipo anamanga misasa yawo pafupi ndi Migidoli.


Nditatulutsa makolo anu ku Igupto ndinafika nawo ku Nyanja Yofiira. Aigupto anawathamangira ndi magaleta ndi okwera pa akavalo mpaka ku Nyanja Yofiira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa