Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 12:45 - Buku Lopatulika

Mlendo kapena wolembedwa ntchito asadyeko.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mlendo kapena wolembedwa ntchito asadyeko.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mlendo kapena wantchito wanu aliyense asadyeko.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma amene mukukhala naye kwa kanthawi kapena waganyu asadye Paska.

Onani mutuwo



Eksodo 12:45
3 Mawu Ofanana  

Ndipo wokhalamo sadzanena, Ine ndidwala; anthu okhala m'menemo, adzakhululukidwa mphulupulu zao.


Mlendo asadyeko chopatulikacho; wakungokhala, ndi wansembe, kapena wolembedwa ntchito, asadyeko chopatulikacho.


kuti nthawi ija munali opanda Khristu, alendo a padera ndi mbumba ya Israele, ndi alendo alibe kanthu ndi mapangano a malonjezano, opanda chiyembekezo, ndi opanda Mulungu m'dziko lapansi.