Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 12:44 - Buku Lopatulika

44 koma kapolo wa mwini aliyense, wogula ndi ndalama, utamdula, ndipo adyeko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

44 koma kapolo wa mwini aliyense, wogula ndi ndalama, utamdula, ndipo adyeko.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

44 Kapolo aliyense wochita kugulidwa angadyeko, koma atayamba waumbalidwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

44 Kapolo aliyense amene munagula angadye ngati atayamba wachita mdulidwe.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 12:44
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu anatenga Ismaele mwana wake ndi onse amene anabadwa m'nyumba mwake, ndi onse amene anagulidwa ndi ndalama zake, amuna onse a mwa anthu a kunyumba kwake kwa Abrahamu, nadula khungu lao tsiku lomwelo, monga Mulungu ananena naye.


Koma wansembe atakagula munthu ndi ndalama zake, iyeyu adyeko; ndi iwo amene anabadwa m'nyumba yake, adyeko mkate wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa