Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 12:44 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

44 Kapolo aliyense amene munagula angadye ngati atayamba wachita mdulidwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

44 koma kapolo wa mwini aliyense, wogula ndi ndalama, utamdula, ndipo adyeko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

44 koma kapolo wa mwini aliyense, wogula ndi ndalama, utamdula, ndipo adyeko.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

44 Kapolo aliyense wochita kugulidwa angadyeko, koma atayamba waumbalidwa.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 12:44
3 Mawu Ofanana  

Tsono Abrahamu anachita mdulidwe mwana wake Ismaeli ndi onse amene anali mʼbanja lake, mbadwa ngakhale kapolo ochita kugula ndi ndalama, monga mmene Mulungu analamulira.


Koma kapolo amene wagulidwa ndi ndalama kapena kubadwira mʼbanja la wansembe angathe kudya chakudya cha wansembeyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa