Eksodo 12:43 - Buku Lopatulika43 Ndipo Yehova anati kwa Mose ndi Aroni, Lemba la Paska ndi ili: mwana wa mlendo aliyense asadyeko; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Ndipo Yehova anati kwa Mose ndi Aroni, Lemba la Paska ndi ili: mwana wa mlendo aliyense asadyeko; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Tsono Chauta adauza Mose ndi Aroni kuti, “Malamulo ake a Paska ndi aŵa: Mlendo aliyense asadyeko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Yehova anati kwa Mose ndi Aaroni, “Malamulo a Paska ndi awa: “Mlendo asadye Paska. Onani mutuwo |