Levitiko 22:10 - Buku Lopatulika10 Mlendo asadyeko chopatulikacho; wakungokhala, ndi wansembe, kapena wolembedwa ntchito, asadyeko chopatulikacho. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Mlendo asadyeko chopatulikacho; wakungokhala, ndi wansembe, kapena wolembedwa ntchito, asadyeko chopatulikacho. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 “Wapadera asadyeko zinthu zopatulika. Mlendo wongokhala nao kwa wansembe, kapena wantchito wake, asadyeko chinthu chopatulika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 “ ‘Aliyense amene si wabanja la wansembe, kaya ndi mlendo wa wansembe, kapena wantchito wake, asadye chopereka chopatulika. Onani mutuwo |