Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 1:6 - Buku Lopatulika

Ndipo anafa Yosefe, ndi abale ake onse, ndi mbadwo uwo wonse.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anafa Yosefe, ndi abale ake onse, ndi mbadwo uwo wonse.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Yosefe adamwalira, abale ake ndi mbadwo wao wonse uja adamwaliranso.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono Yosefe ndi abale ake onse ndiponso mʼbado wawo wonse anamwalira.

Onani mutuwo



Eksodo 1:6
5 Mawu Ofanana  

Yosefe ndipo anati kwa abale ake, Ndilinkufa ine, koma Mulungu adzaonekera kwa inu, adzakuchotsani inu m'dziko muno kubwera kunka ku dziko limene analumbirira kwa Abrahamu ndi kwa Isaki, ndi kwa Yakobo.


Ndipo anafa Yosefe, anali wa zaka zana limodzi ndi khumi; ndipo anakonza thupi lake ndi mankhwala osungira, ndipo anamuika iye m'bokosi mu Ejipito.


Mbadwo wina upita, mbadwo wina nufika; koma dziko lingokhalabe masiku onse.


Ndiponso mbadwo uwu wonse unasonkhanidwa kuikidwa kwa makolo ao; nuuka mbadwo wina pambuyo pao; wosadziwa Yehova kapena ntchitoyi adaichitira Israele.