Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Danieli 7:3 - Buku Lopatulika

Ndipo zinatuluka m'nyanja zilombo zazikulu zinai zosiyanasiyana.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo zinatuluka m'nyanja zilombo zazikulu zinai zosiyanasiyana.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo mʼnyangayo munatuluka zirombo zazikulu zinayi, chilichonse chosiyana ndi chinzake.

Onani mutuwo



Danieli 7:3
9 Mawu Ofanana  

Inu ndinu wakuunikira, ndi womveka wakuposa mapiri muli achifwamba.


Zilombo zazikulu izi zinai ndizo mafumu anai amene adzauka padziko lapansi.


Ndipo ndinaimirira pa mchenga wa nyanja. Ndipo ndinaona chilombo chilinkutuluka m'nyanja, chakukhala nazo nyanga khumi, ndi mitu isanu ndi iwiri, ndi pa nyanga zake nduwira zachifumu khumi, ndi pamitu pake maina a mwano.


Chilombo chimene unachiona chinaliko, koma kulibe; ndipo chidzatuluka m'chiphompho chakuya, ndi kunka kuchitayiko. Ndipo adzazizwa iwo akukhala padziko amene dzina lao silinalembedwe m'buku la moyo chiyambire makhazikidwe a dziko lapansi, pakuona chilombo, kuti chinaliko, ndipo kulibe, ndipo chidzakhalako.