Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Danieli 5:27 - Buku Lopatulika

TEKEL, Mwayesedwa pamiyeso, nimupezeka mwaperewera.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

TEKEL, Mwayesedwa pamiyeso, nimupezeka mwaperewera.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tekeli: Inu mwayesedwa pa sikelo ndipo mwapezeka kuti mukuperewera.

Onani mutuwo



Danieli 5:27
10 Mawu Ofanana  

andiyese ndi muyeso wolingana, kuti Mulungu adziwe ungwiro wanga.


Indetu, anthu achabe ndi mpweya, ndipo anthu aakulu ndi bodza, pakuwayesa apepuka; onse pamodzi apepuka koposa mpweya.


Njira zonse za munthu ziyera pamaso pake; koma Yehova ayesa mizimu.


Njira zonse za munthu zilungama pamaso pake; koma Yehova ayesa mitima.


Anthu adzawatcha nthale ya siliva, pakuti Yehova wakana iwo.


Ndipo iwe wobadwa ndi munthu, udzitengere mpeni wakuthwa, ndiwo lumo la wometa, udzitengere ndi kulipititsa pamutu pako ndi pa ndevu zako; nudzitengere muyeso kuyesa nao, ndi kugawa tsitsilo.


Ndipo Yehova walamulira za iwe kuti asabzalidwenso ena a dzina lako; m'nyumba ya milungu yako ndidzachotsa fano losema ndi fano loyenga; ndidzakukonzerapo manda, pakuti iwe ndiwe wopepuka.


ntchito ya yense idzaonetsedwa; pakuti tsikulo lidzaisonyeza, chifukwa kuti yavumbululuka m'moto; ndipo moto wokha udzayesera ntchito ya yense ikhala yotani.