Yeremiya 6:30 - Buku Lopatulika30 Anthu adzawatcha nthale ya siliva, pakuti Yehova wakana iwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Anthu adzawatcha nthale ya siliva, pakuti Yehova wakana iwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Iwo ali ngati siliva wotaya, pakuti Chauta waŵakana.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Iwo ali ngati siliva wotayidwa, chifukwa Yehova wawakana.” Onani mutuwo |