Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 6:30 - Buku Lopatulika

30 Anthu adzawatcha nthale ya siliva, pakuti Yehova wakana iwo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Anthu adzawatcha nthale ya siliva, pakuti Yehova wakana iwo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Iwo ali ngati siliva wotaya, pakuti Chauta waŵakana.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Iwo ali ngati siliva wotayidwa, chifukwa Yehova wawakana.”

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 6:30
16 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anakaniza mbumba yonse ya Israele, nawazunza, nawapereka m'dzanja la ofunkha, mpaka anawataya pamaso pake.


Muchotsa oipa onse a padziko lapansi ngati mphala: Chifukwa chake ndikonda mboni zanu.


Pamenepo anaopa kwakukulu, popanda chifukwa cha kuopa, pakuti Mulungu anamwaza mafupa a iwo akuzinga iwe; unawachititsa manyazi, pakuti Mulungu anawakaniza.


Chotsera siliva mphala yake, mmisiri wa ng'anjo atulutsamo mbale.


Siliva wako wasanduka mphala, vinyo wako wasakanizidwa ndi madzi.


ndipo ndidzaikanso dzanja langa pa iwe, ndi kukusungunula kukusiyanitsa iwe ndi mphala yako, ndipo ndidzachotsa seta wako wonse:


Kodi mwakanadi Yuda? Kodi mtima wanu wanyansidwa ndi Ziyoni? Bwanji mwatipanda ife, ndipo tilibe kuchira? Tinayembekeza mtendere, koma sizinafike zabwino; tinayembekeza nthawi yakuchira, ndipo taonani mantha!


Ndipo pamene anthu awa, kapena mneneri, kapena wansembe, adzakufunsa iwe, kuti, Katundu wa Yehova ndi chiyani? Pamenepo uziti kwa iwo, Katundu wanji? Ndidzakuchotsani inu, ati Yehova.


Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti,


Meta tsitsi lako, iwe Yerusalemu, nulitaye, nukweze maliro pa mapiri oti see; pakuti Yehova wakana ndi kusiya mbadwo umene aukwiyira.


Koma mwatikaniza konse, mwatikwiyira kopambana.


Mulungu wanga adzawataya, pakuti sanammvere Iye; ndipo adzakhala othawathawa mwa amitundu.


Ndipo ndinatha abusa atatuwo mwezi umodzi; pakuti mtima wanga unalema nao, ndi mtima waonso unaipidwa nane.


Inu ndinu mchere wa dziko lapansi; koma mcherewo ngati ukasukuluka, adzaukoleretsa ndi chiyani? Pamenepo sungakwanirenso kanthu konse, koma kuti ukaponyedwe kunja, nupondedwe ndi anthu.


Chifukwa chake ndinena, Mulungu anataya anthu ake kodi? Msatero ai. Pakuti inenso ndili Mwisraele, wa mbeu ya Abrahamu, wa fuko la Benjamini.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa