Danieli 5:28 - Buku Lopatulika28 PERES, ufumu wanu wagawika, nuperekedwa kwa Amedi ndi Aperisi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 PERES, ufumu wanu wagawika, nuperekedwa kwa Amedi ndi Aperisi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Parasini: Ufumu wanu wagawidwa ndi kupatsidwa kwa Amedi ndi Aperezi.” Onani mutuwo |