Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Danieli 5:27 - Buku Lopatulika

27 TEKEL, Mwayesedwa pamiyeso, nimupezeka mwaperewera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 TEKEL, Mwayesedwa pamiyeso, nimupezeka mwaperewera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Tekeli: Inu mwayesedwa pa sikelo ndipo mwapezeka kuti mukuperewera.

Onani mutuwo Koperani




Danieli 5:27
10 Mawu Ofanana  

andiyese ndi muyeso wolingana, kuti Mulungu adziwe ungwiro wanga.


Indetu, anthu achabe ndi mpweya, ndipo anthu aakulu ndi bodza, pakuwayesa apepuka; onse pamodzi apepuka koposa mpweya.


Njira zonse za munthu ziyera pamaso pake; koma Yehova ayesa mizimu.


Njira zonse za munthu zilungama pamaso pake; koma Yehova ayesa mitima.


Anthu adzawatcha nthale ya siliva, pakuti Yehova wakana iwo.


Ndipo iwe wobadwa ndi munthu, udzitengere mpeni wakuthwa, ndiwo lumo la wometa, udzitengere ndi kulipititsa pamutu pako ndi pa ndevu zako; nudzitengere muyeso kuyesa nao, ndi kugawa tsitsilo.


Ndipo Yehova walamulira za iwe kuti asabzalidwenso ena a dzina lako; m'nyumba ya milungu yako ndidzachotsa fano losema ndi fano loyenga; ndidzakukonzerapo manda, pakuti iwe ndiwe wopepuka.


ntchito ya yense idzaonetsedwa; pakuti tsikulo lidzaisonyeza, chifukwa kuti yavumbululuka m'moto; ndipo moto wokha udzayesera ntchito ya yense ikhala yotani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa