Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Danieli 4:28 - Buku Lopatulika

Chonsechi chinagwera mfumu Nebukadinezara.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chonsechi chinagwera mfumu Nebukadinezara.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Zonsezi zinamuchitikira mfumu Nebukadinezara.

Onani mutuwo



Danieli 4:28
5 Mawu Ofanana  

Chomwe woipa achiopa chidzamfikira; koma chomwe olungama achifuna chidzapatsidwa.


Koma pokwezeka mtima wake, nulimba mzimu wake kuchita modzikuza, anamtsitsa pa mpando wa ufumu wake, namchotsera ulemerero wake;


Koma mau anga ndi malemba anga, amene ndinalamulira atumiki anga aneneriwo, kodi sanawapeze makolo anu? Ndipo anabwera, nati, Monga umo Yehova wa makamu analingirira kutichitira ife, monga mwa njira zathu ndi monga mwa machitidwe athu, momwemo anatichitira.


Mulungu sindiye munthu, kuti aname; kapena mwana wa munthu, kuti aleke; kodi anena, osachita?


Thambo ndi dziko lapansi zidzachoka, koma mau anga sadzachoka ai.