Numeri 23:19 - Buku Lopatulika19 Mulungu sindiye munthu, kuti aname; kapena mwana wa munthu, kuti aleke; kodi anena, osachita? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Mulungu sindiye munthu, kuti aname; kapena mwana wa munthu, kuti aleke; kodi anena, osachita? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Mulungu sali ngati munthu kuti angathe kunama, si munthu kuti angathe kusintha maganizo ake. Kodi sadzachitadi zomwe adanena? Kapena sadzachitadi zimene adalankhula? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Mulungu si munthu kuti aname, kapena mwana wa munthu kuti asinthe maganizo ake. Kodi amayankhula koma osachita? Kodi amalonjeza koma osakwaniritsa? Onani mutuwo |