Danieli 4:29 - Buku Lopatulika29 Itatha miyezi khumi ndi iwiri, analikuyenda m'chinyumba chachifumu cha ku Babiloni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Itatha miyezi khumi ndi iwiri, analikuyenda m'chinyumba chachifumu cha ku Babiloni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Itapita miyezi khumi ndi iwiri, pamene mfumu inkayenda pa denga la nyumba ya ufumu ya ku Babuloni, Onani mutuwo |