Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Danieli 4:28 - Buku Lopatulika

28 Chonsechi chinagwera mfumu Nebukadinezara.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Chonsechi chinagwera mfumu Nebukadinezara.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Zonsezi zinamuchitikira mfumu Nebukadinezara.

Onani mutuwo Koperani




Danieli 4:28
5 Mawu Ofanana  

Chomwe woipa achiopa chidzamfikira; koma chomwe olungama achifuna chidzapatsidwa.


Koma pokwezeka mtima wake, nulimba mzimu wake kuchita modzikuza, anamtsitsa pa mpando wa ufumu wake, namchotsera ulemerero wake;


Koma mau anga ndi malemba anga, amene ndinalamulira atumiki anga aneneriwo, kodi sanawapeze makolo anu? Ndipo anabwera, nati, Monga umo Yehova wa makamu analingirira kutichitira ife, monga mwa njira zathu ndi monga mwa machitidwe athu, momwemo anatichitira.


Mulungu sindiye munthu, kuti aname; kapena mwana wa munthu, kuti aleke; kodi anena, osachita?


Thambo ndi dziko lapansi zidzachoka, koma mau anga sadzachoka ai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa