Mateyu 24:35 - Buku Lopatulika35 Thambo ndi dziko lapansi zidzachoka, koma mau anga sadzachoka ai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Thambo ndi dziko lapansi zidzachoka, koma mau anga sadzachoka ai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Thambo ndi dziko lapansi zidzatha, koma mau anga sadzatha mphamvu konse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Kumwamba ndi dziko lapansi zidzatha, koma mawu anga sadzatha.” Onani mutuwo |