Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Akolose 4:4 - Buku Lopatulika

kuti ndichionetse ichi monga ndiyenera kulankhula.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

kuti ndichionetse ichi monga ndiyenera kulankhula.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mundipempherere tsono kuti ndichifotokoze bwino monga ndiyenera.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pempherani kuti ndilalikire momveka bwino, monga ndikuyenera.

Onani mutuwo



Akolose 4:4
10 Mawu Ofanana  

Ndipo tsopano Ambuye, penyani mau ao akuopsa, ndipo patsani kwa akapolo anu alankhule mau anu ndi kulimbika mtima konse,


Ndipo anayankha Petro ndi atumwi, nati, Tiyenera kumvera Mulungu koposa anthu.


Pokhala nacho tsono chiyembekezo chotere, tilankhula ndi kukhazikika mtima kwakukulu,


chifukwa cha umene ndili mtumiki wa mu unyolo, kuti m'menemo ndikalankhule molimbika, monga ndiyenera kulankhula.


Muyendere munzeru ndi iwo akunja, kuchita machawi nthawi ingatayike.


Mau anu akhale m'chisomo, okoleretsa, kuti mukadziwe inu mayankhidwe anu a kwa yense akatani.