Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Ahebri 11:2 - Buku Lopatulika

Pakuti momwemo akulu anachitidwa umboni.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti momwemo akulu anachitidwa umboni.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pokhala ndi chikhulupiriro, makolo anthu akale aja Mulungu adaonetsa kuti ankakondwera nawo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndi chikhulupiriro chimenechi makolo athu akale anayamikidwa.

Onani mutuwo



Ahebri 11:2
3 Mawu Ofanana  

Kale Mulungu analankhula ndi makolo mwa aneneri m'manenedwe ambiri ndi mosiyanasiyana,


Ndipo iwo onse adachitidwa umboni mwa chikhulupiriro, sanalandire lonjezanolo,


Ndi chikhulupiriro Abele anapereka kwa Mulungu nsembe yoposa ija ya Kaini, imene anachitidwa umboni nayo kuti anali wolungama; nachitapo umboni Mulungu pa mitulo yake; ndipo momwemo iye, angakhale adafa alankhulabe.