Ahebri 11:1 - Buku Lopatulika1 Koma chikhulupiriro ndicho chikhazikitso cha zinthu zoyembekezeka, chiyesero cha zinthu zosapenyeka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Koma chikhulupiriro ndicho chikhazikitso cha zinthu zoyembekezeka, chiyesero cha zinthu zosapenyeka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tikati kukhulupirira, ndiye kuti kusakayika konse pa zinthu zimene tikuziyembekeza, ndiponso kutsimikiza kuti zinthu zimene sitikuziwona zilipo ndithu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tsopano chikhulupiriro ndi kusakayika konse pa zinthu zimene tikuziyembekeza, ndi kutsimikiza kuti zinthu zimene sitiziona zilipo ndithu. Onani mutuwo |