Ahebri 11:2 - Buku Lopatulika2 Pakuti momwemo akulu anachitidwa umboni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Pakuti momwemo akulu anachitidwa umboni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Pokhala ndi chikhulupiriro, makolo anthu akale aja Mulungu adaonetsa kuti ankakondwera nawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndi chikhulupiriro chimenechi makolo athu akale anayamikidwa. Onani mutuwo |