Ahebri 1:1 - Buku Lopatulika1 Kale Mulungu analankhula ndi makolo mwa aneneri m'manenedwe ambiri ndi mosiyanasiyana, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Kale Mulungu analankhula ndi makolo mwa aneneri m'manenedwe ambiri ndi mosiyanasiyana, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Kale lija pa nthaŵi zosiyanasiyana, mwa njira zosiyanasiyana, Mulungu adaalankhula ndi makolo athu kudzera mwa aneneri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Kale lija Mulungu ankayankhula ndi makolo athu pa nthawi zosiyanasiyana ndiponso mwa njira zosiyanasiyana kudzera mwa aneneri. Onani mutuwo |