Ahebri 11:39 - Buku Lopatulika39 Ndipo iwo onse adachitidwa umboni mwa chikhulupiriro, sanalandire lonjezanolo, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Ndipo iwo onse adachitidwa umboni mwa chikhulupiriro, sanalandira lonjezanolo, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Anthu onseŵa, ngakhale adaaŵachitira umboni wokoma chifukwa cha chikhulupiriro chao, sadalandire zimene Mulungu adaalonjeza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Onsewa anayamikidwa chifukwa cha chikhulupiriro chawo, komabe palibe wa iwo amene analandira zimene analonjezedwa. Onani mutuwo |