Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Afilipi 1:3 - Buku Lopatulika

Ndiyamika Mulungu wanga pokumbukira inu ponse;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndiyamika Mulungu wanga pokumbukira inu ponse;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndimayamika Mulungu wanga nthaŵi zonse ndikamakukumbukirani.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndimayamika Mulungu wanga nthawi zonse ndikakumbukira inu.

Onani mutuwo



Afilipi 1:3
10 Mawu Ofanana  

Koma ayamikidwe Mulungu, kuti ngakhale mudakhala akapolo a uchimo, tsopano mwamvera ndi mtima makhalidwe aja a chiphunzitso chimene munaperekedweracho;


Ndiyamika Mulungu wanga nthawi yonse kaamba ka inu, chifukwa cha chisomo cha Mulungu chinapatsidwa kwa inu mwa Khristu Yesu;


Pakuti tikhoza kubwezera kwa Mulungu chiyamiko chanji chifukwa cha inu, pa chimwemwe chonse tikondwera nacho mwa inu pamaso pa Mulungu wathu;


Tiziyamika Mulungu nthawi zonse chifukwa cha inu, abale, monga kuyenera; pakuti chikhulupiriro chanu chikula chikulire, ndipo chichulukira chikondano cha inu nonse, yense pa mnzake;


Ndiyamika Mulungu, amene ndimtumikira kuyambira makolo anga ndi chikumbumtima choyera, kuti ndikumbukira iwe kosalekeza m'mapemphero anga,